Skip to content

Malawi Cables Online

We Report the Future — the Only Trusted Source of News with a Difference

Primary Menu
  • Home
  • Latest
  • News
  • Breaking News
  • Religion
  • Economics
  • Politics
  • Sports
  • Home
  • Blog
  • Home
  • Latest
  • Aphungu Khumi a Chipani cha MCP Akufuna Mtsogoleri Wakale A Chakwera, Adzayimilenso mu 2030
  • Latest
  • Politics

Aphungu Khumi a Chipani cha MCP Akufuna Mtsogoleri Wakale A Chakwera, Adzayimilenso mu 2030

Malawi Cables July 26, 2026 (Last updated: July 26, 2026)
IMG_5342

Pomwe kuli khwimbi la mundipondela mwana pa bwalo lamasewero la Sukulu ya Pulayimale ya Malembo, pomwe phungu wa dera la Lilongwe Chilobwe, a Lawrence Chakakala Chaziya, akuchititsa msonkhano wa ndale.

Aphungu a chipani chotsutsa cha Malawi Congress Party (MCP) oposa khumi ochokera m’madera osiyanasiyana omwe ali nawo pa msonkhanowu, ati akufuna mtsogoleri wakale wa dziko lino, yemwenso ndi mtsogoleri wa chipani cha MCP, a Lazarus Chakwera, adzayimile chipanichi mu masankho a 2030.

Aphungu onse omwe ali pamsonkhanowu ati mtsogoleri wa chipanichi, a Lazarus Chakwera, akufunidwa kuti adzayimilenso mchaka cha 2030 ndi anthu ambiri m’madera awo.

“Anthu m’madera athu akuti akufuna a Chakwera adzayimilenso mu 2030, ndipo tati a Malawi mudziwe zimenezi,” atero aphungu angapo.

Ena mwa aphunguwa adzudzulanso boma lolamula la DPP chifukwa chosaganizira mavuto ena omwe a Malawi akukumana nawo.

“Inde chimanga chikupezeka ndipo chakudya sichikusowa, koma a Malawi ali ndi mavuto ambiri,” anatero a Chaziya.

Mwa zina, aphunguwa anadandaula za kukwera kwa mitengo ya feteleza, kukwera kwa fizi m’makoleji, mitengo yotsika ya mbewu, ndi mavuto ena.

Aphungu enanso anati boma mwina lichepetse ndalama za CDF kufika pa mulingo umene lingakwanitse, chifukwa pakali pano palibe chilipo.

About the Author

Malawi Cables

Administrator

Malawi Cables is a dedicated news platform committed to delivering timely, accurate, and credible coverage of events and stories from Malawi and beyond. We aim to inform, educate, and engage our readers through in-depth reporting, insightful analysis, and impactful storytelling that sets us apart.

Visit Website View All Posts

Like this:

Like Loading…

Related

Post navigation

Previous: Mangochi Districts Hospital Called For More Awareness Campaings As Children With Cerebral Palsy Still Faces Rejections In Some Communities
Next: Chakwera Was Surrounded by Crooks Who Misled Him — Malondera Speaks

Related Stories

IMG_6790
  • Latest

DPP Has Managed To Solve Part Of The Mess Created By MCP: Mukhito

Malawi Cables September 13, 2026
IMG_6789
  • Latest

MCP Back To Its Senses: Admits It Cannot Beat DPP Alone, Apologises To UTM, Other Tonse Alliance Parties

Malawi Cables September 13, 2026
1000095407
  • Latest

10 People Arrested In Dowa For Damaging Property And Unlawful Wounding

Andy Ten September 13, 2026

Recent Posts

  • DPP Has Managed To Solve Part Of The Mess Created By MCP: Mukhito
  • MCP Back To Its Senses: Admits It Cannot Beat DPP Alone, Apologises To UTM, Other Tonse Alliance Parties
  • 10 People Arrested In Dowa For Damaging Property And Unlawful Wounding
  • 40 Years-old Woman Dies While Searching For Gold In Lilongwe
  • APM Calls For Stronger Government–Private Sector Partnership

Recent Comments

No comments to show.

Archives

  • September 2026
  • August 2026
  • July 2026
  • June 2026
  • May 2026
  • April 2026
  • March 2026
  • February 2026
  • January 2026
  • December 2025

Categories

  • Breaking News
  • Economics
  • Home
  • Latest
  • News
  • Politics
  • Religion
  • Sports

You May Have Missed

IMG_6790
  • Latest

DPP Has Managed To Solve Part Of The Mess Created By MCP: Mukhito

Malawi Cables September 13, 2026
IMG_6789
  • Latest

MCP Back To Its Senses: Admits It Cannot Beat DPP Alone, Apologises To UTM, Other Tonse Alliance Parties

Malawi Cables September 13, 2026
1000095407
  • Latest

10 People Arrested In Dowa For Damaging Property And Unlawful Wounding

Andy Ten September 13, 2026
1000170947
  • Latest

40 Years-old Woman Dies While Searching For Gold In Lilongwe

Andy Ten September 12, 2026
Copyright © 2026 All rights reserved. | ReviewNews by AF themes.
%d