Skip to content

Malawi Cables Online

We Report the Future — the Only Trusted Source of News with a Difference

Primary Menu
  • Home
  • Latest
  • News
  • Breaking News
  • Religion
  • Economics
  • Politics
  • Sports
  • Home
  • Blog
  • Home
  • Latest
  • Dr. Chakwera Akhala Nawo Pa Mwambo Wa Maliro a Professor Zimani Kadzamila Ku Dedza
  • Latest

Dr. Chakwera Akhala Nawo Pa Mwambo Wa Maliro a Professor Zimani Kadzamila Ku Dedza

Andy Ten September 20, 2026 (Last updated: September 20, 2026)

Pulezidenti wachisanu ndi chimodzi wa dziko lino Dr Lazarus McCarthy Chakwera akuyembekezereka kukhala nawo pa mwambo oyika mmanda thupi la malemu Zimani Kadzamila amene anamwalira lachisanu lapitali.

Malingana ndi chikalata chomwe wasayinila mneneri wa mtsogoleri wakaleyu a Gift Nankhuni Dr Chakwera apita ku mwambowu pamodzi ndi mayi wakale wafuko lino a Monica Chakwera.

A Chakwera akuyembekezeleka kufika ku mwambowu womwe uchitikile ku Linthipe , m’boma la Dedza nthawi ya 9 koloko mamawa.

Professor Zimani Kadzamila adali kaswiri wazamaphunziro ndi adakhalapo wachiwiri kwa Mkulu wa Sukulu ya Ukachenjede ya Malawi komanso adali mchimwene wawo wa mayi Cecilia Kadzamila.

About the Author

Andy Ten

Editor

Journalist from Mangochi former student and University of Malawi, The Polytechnic

View All Posts

Like this:

Like Loading…

Related

Post navigation

Previous: Apolisi Asanu Ndi Atatu Apasidwa K1 Miliyoni Komanso Kukwedzedwa Ma Udindo Kaamba Kodzipeleka Pa Ntchito
Next: Two Men Arrested In Mchinji For Breaking Into Mkanda Assembliess Of God Church And Stealing Sound Equipments

Related Stories

1000104406
  • Latest

Two Men Arrested In Mchinji For Breaking Into Mkanda Assembliess Of God Church And Stealing Sound Equipments

Andy Ten September 20, 2026
1000103669
  • Latest

Apolisi Asanu Ndi Atatu Apasidwa K1 Miliyoni Komanso Kukwedzedwa Ma Udindo Kaamba Kodzipeleka Pa Ntchito

Andy Ten September 19, 2026
Screenshot
  • Latest

MONEY-LAUNDERING SUSPECT SHABBIR RAIDHAN RELOCATES TO UK AS MALAWI HOUSE GOES ON SALE, CASE IN COURT HANGS IN BALANCE

Malawi Cables September 19, 2026

Recent Posts

  • Two Men Arrested In Mchinji For Breaking Into Mkanda Assembliess Of God Church And Stealing Sound Equipments
  • Dr. Chakwera Akhala Nawo Pa Mwambo Wa Maliro a Professor Zimani Kadzamila Ku Dedza
  • Apolisi Asanu Ndi Atatu Apasidwa K1 Miliyoni Komanso Kukwedzedwa Ma Udindo Kaamba Kodzipeleka Pa Ntchito
  • MONEY-LAUNDERING SUSPECT SHABBIR RAIDHAN RELOCATES TO UK AS MALAWI HOUSE GOES ON SALE, CASE IN COURT HANGS IN BALANCE
  • LABOUR MINISTRY RECRUITING FOR ISRAEL JOBS SECRETLY: PARTY CADRES, RELATIVES FIRST

Recent Comments

No comments to show.

Archives

  • September 2026
  • August 2026
  • July 2026
  • June 2026
  • May 2026
  • April 2026
  • March 2026
  • February 2026
  • January 2026
  • December 2025

Categories

  • Breaking News
  • Economics
  • Home
  • Latest
  • News
  • Politics
  • Religion
  • Sports

You May Have Missed

1000104406
  • Latest

Two Men Arrested In Mchinji For Breaking Into Mkanda Assembliess Of God Church And Stealing Sound Equipments

Andy Ten September 20, 2026
1000104013
  • Latest

Dr. Chakwera Akhala Nawo Pa Mwambo Wa Maliro a Professor Zimani Kadzamila Ku Dedza

Andy Ten September 20, 2026
1000103669
  • Latest

Apolisi Asanu Ndi Atatu Apasidwa K1 Miliyoni Komanso Kukwedzedwa Ma Udindo Kaamba Kodzipeleka Pa Ntchito

Andy Ten September 19, 2026
Screenshot
  • Latest

MONEY-LAUNDERING SUSPECT SHABBIR RAIDHAN RELOCATES TO UK AS MALAWI HOUSE GOES ON SALE, CASE IN COURT HANGS IN BALANCE

Malawi Cables September 19, 2026
Copyright © 2026 All rights reserved. | ReviewNews by AF themes.
%d