Skip to content

Malawi Cables Online

We Report the Future — the Only Trusted Source of News with a Difference

Primary Menu
  • Home
  • Latest
  • News
  • Breaking News
  • Religion
  • Economics
  • Politics
  • Sports
  • Home
  • Blog
  • Home
  • Latest
  • Bambo Wa Zaka 21 Wazipha Pomwa Poizoni Ku Machinga Kamba Ka K50,000 Yomwe Mchimwene Wake Samamubwezera
  • Latest

Bambo Wa Zaka 21 Wazipha Pomwa Poizoni Ku Machinga Kamba Ka K50,000 Yomwe Mchimwene Wake Samamubwezera

Andy Ten September 5, 2026 (Last updated: September 5, 2026)

Bambo wina a Chikondi Mavuto a zaka 21 apezeka atafa kutchire atamwa poizoni m’boma la Machinga.

Malingana ndi Ofalitsa nkhani za Polisi m’boma la Machinga a Western Kansire anthu anapeza thupi la a Mavuto pa 4 September 2026 nthawi ya 6 koloko mamawa mmudzi mwa a Masaka m’bomali.

Kansire wati a Mavuto anamubwereka mchimwene wawo K50,000 ndipo malemuwa samabwezeredwa ndaalamayo ngakhale amakakumbusa zangongoleyo pafupipafupi.

“Pa 1 September malemuwa anapitanso kwa mchimwene wawo kokumbutsa ndalamayo ndipo awiriwa anakangana kwambiri. Izi zinapangitsa a Mavuto kudandaulira mzawo wapamtima za khalidwe la mchimwene wawo komanso lingaliro lawo lofuna kuzipha,” watero Kansire.

Pa 4 September ndipamene a Mavuto anapezeka atamwalira komanso thupi lawo linali litaonongekaratu popeza linali litapsanso ndi moto wa mtchire ndipo azimayi omwe amasaka nkhuni ndi amene anapeza thupi la malemuwa.

A Polisi ya Ntaja komanso akadaulo azachipatala atathamangira kumalo angoziwo ndipo atachita kafukufuku apeza zoti imfa ya malemuwo inaza kaamba kakumwa poizoni.

Apa apolisi apempha anthu kuti azipempha uphungu ku Polisi ndi malo ena oyenera akakhala kuti akumana ndi mavuto mmoyo wawo

A chikondi Mavuto anali ochokera mmudzi mwa Masaka , Mfumu yaikulu Liwonde, m’boma lomweli la Machinga.

Chithunzii ndi cha AI generated

About the Author

Andy Ten

Editor

Journalist from Mangochi former student and University of Malawi, The Polytechnic

View All Posts

Like this:

Like Loading…

Related

Post navigation

Previous: Simba Sporting Club Donate Groceries To The Ministry of Hope Crisis Nursery In Lilongwe

Related Stories

1000164408
  • Latest

Simba Sporting Club Donate Groceries To The Ministry of Hope Crisis Nursery In Lilongwe

Andy Ten September 5, 2026
Screenshot
  • Latest

DPP’s 2025 Win: What Delivered Victory and What Could Cost Them in 2030

Malawi Cables September 5, 2026
Screenshot
  • Latest

DPP VS PARLIAMENT: CDEDI RALLIES BEHIND SULEMAN, DEMANDS AN END TO INTIMIDATION

Malawi Cables September 4, 2026

Recent Posts

  • Bambo Wa Zaka 21 Wazipha Pomwa Poizoni Ku Machinga Kamba Ka K50,000 Yomwe Mchimwene Wake Samamubwezera
  • Simba Sporting Club Donate Groceries To The Ministry of Hope Crisis Nursery In Lilongwe
  • DPP’s 2025 Win: What Delivered Victory and What Could Cost Them in 2030
  • DPP VS PARLIAMENT: CDEDI RALLIES BEHIND SULEMAN, DEMANDS AN END TO INTIMIDATION
  • POLICE ARREST A PRIMARY SCHOOL TEACHER IN KASUNGU FOR FORGING HIS DEATH DOCUMENTS TO RUN AWAY FROM PAYING BACK HIS OUTSTANDING LOAN

Recent Comments

No comments to show.

Archives

  • September 2026
  • August 2026
  • July 2026
  • June 2026
  • May 2026
  • April 2026
  • March 2026
  • February 2026
  • January 2026
  • December 2025

Categories

  • Breaking News
  • Economics
  • Home
  • Latest
  • News
  • Politics
  • Religion
  • Sports

You May Have Missed

1000164451
  • Latest

Bambo Wa Zaka 21 Wazipha Pomwa Poizoni Ku Machinga Kamba Ka K50,000 Yomwe Mchimwene Wake Samamubwezera

Andy Ten September 5, 2026
1000164408
  • Latest

Simba Sporting Club Donate Groceries To The Ministry of Hope Crisis Nursery In Lilongwe

Andy Ten September 5, 2026
Screenshot
  • Latest

DPP’s 2025 Win: What Delivered Victory and What Could Cost Them in 2030

Malawi Cables September 5, 2026
Screenshot
  • Latest

DPP VS PARLIAMENT: CDEDI RALLIES BEHIND SULEMAN, DEMANDS AN END TO INTIMIDATION

Malawi Cables September 4, 2026
Copyright © 2026 All rights reserved. | ReviewNews by AF themes.
%d