Mbava Ndi Zomwezi As MCP Wants To Steal K1 Trillion In Bogus Fuel Deals

Nkhani ili pamudzi pano ndiyakuti ku bomako anapangana kuti atibere K1 trillion ife Amalawi m’dzina la kugula mafuta.

Anapanga kakampani kawo kabodzabodza ndikukatsekula akaunti ku Banki, ali ndalama zizidutsira kumeneko. Nkhanga zaona.

N’chifukwa chake lero manyuzipepala akulu-akulu onse alemba za nkhaniyi, yomwe woyamba kulemba anali a The Investigator magazine. Umbava wopanda nawo manyazi.

Malawi Cables

Malawi Cables is a dedicated news platform providing timely and accurate coverage of events and stories from Malawi and beyond. The website aims to inform and engage readers by delivering powerful analysis and reporting.

Related Posts

Leave a Reply

You Missed

SLEEPY, PUPPET CHAKWERA BOWS TO SON’S PRESSURE, EYES MUMBA AS RUNNING MATE, 2030 SUCCESSOR

SLEEPY, PUPPET CHAKWERA BOWS TO SON’S PRESSURE, EYES MUMBA AS RUNNING MATE, 2030 SUCCESSOR

Usi Sparks Outrage at Mulli Funeral: Accused of Turning Burial into Political Stage

Usi Sparks Outrage at Mulli Funeral: Accused of Turning Burial into Political Stage

Mutharika Criticizes Faith Community’s Silence on Governance Amid National Hardships

Mutharika Criticizes Faith Community’s Silence on Governance Amid National Hardships

“Chakwera Can’t Fire Me,” Boasts Chimwendo Banda

“Chakwera Can’t Fire Me,” Boasts Chimwendo Banda