DK Pays MK 20 Million Nomination Fee For UTM Presidency

Times360Malawi

A Kabambe omwe apeleka cheke cha K20 million ati nthumwi zikawavotere chifukwa iwo all ndi ukadaulo oyendetsa chuma cha chipani komanso cha dziko.

A Kabambe omwe anali mkulu wa banki yaikulu ya dziko lino ati boma lomwe lilipo pakadali pano lalephera kuyendetsa chuma cha dziko.

“Panopa osauka akusaukirabe, anthu alibe chakudya. Mvulanso yayamba koma alibe feteleza. Omwe ali ndi galimoto ndiye akugona mma filling station nawo mavuto okhaokha. This government is clueless, it doesn’t know a anything and that’s why they say running government is not for babies,” atero a Kabambe.

A Kabambe, atinnso anthu mu chipani cha UTM abwere pamodzi ndikupanga kampeni yovuta kuti chaka cha mawa atenge boma.

“Amalawi ayesapo zipani zina, zalephera. Pano yesani UTM. Ine Dalitso Kabambe lero ndapeleka zikalata zosonyeza chidwi kupikisana, ndili ndi ukadaulo oyendetsa chuma cha dziko ndipo zinthu zambiri zomwe boma ili likupanga molakwikwa, mayankho ake ndili nawo,” atero a Kabambe.

Malawi Cables

Malawi Cables is a dedicated news platform providing timely and accurate coverage of events and stories from Malawi and beyond. The website aims to inform and engage readers by delivering powerful analysis and reporting.

Related Posts

Leave a Reply

You Missed

Malawi Awards Multimillion $ Passport Printing Contract To A Blacklisted Coy

Malawi Awards Multimillion $ Passport Printing Contract To A Blacklisted Coy

DPP’ Gangata Dates Dwangwa As He Takes Over MCP’ Bases

DPP’ Gangata Dates Dwangwa As He Takes Over MCP’ Bases

MEC Spends K23 Million Shipping Election Materials to Panama Amid Smartmatic Controversy

MEC Spends K23 Million Shipping Election Materials to Panama Amid Smartmatic Controversy

‘ IG ‘Ackis Muwanga Eliminates Opponents Ahead of Malawi Police Easter Promotions

‘ IG ‘Ackis Muwanga Eliminates Opponents Ahead of Malawi Police Easter Promotions