Chakwera’a Bloody Maize Donation Claims Life of Seven

A Polisi ya Ndirande mu mzinda wa Blantyre ati anthu okwana 7 ndi omwe amwalira pa ngozi imene yachitika mu msewu wa Magalasi chaku madzuloku.

Anthuwa amachokera ku bwalo la masewero la Kamuzu kumene adakalandira chimanga chimene bungwe la Dodma likupereka kwa anthu.

Malinga ndi wofalitsa nkhani pa polisi ya Ndirande a Maxwell Jailosi, galimotoyi idanyamula anthu okwana 37 ndipo mwa anthuwa awiri ndi amene avulala modetsa nkhawa pamene asanu awathandiza ndipo awatulutsa.

Galimoto ya mtundu wa lorry limene anthuwa adakwera, malinga ndi amene adaona izi zikuchitika a Isaac Chilenje, lidaonongeka mabuleki zimene zidachititsa kuti lithamange kwambiri lisadagwe.

Malawi Cables

Malawi Cables is a dedicated news platform providing timely and accurate coverage of events and stories from Malawi and beyond. The website aims to inform and engage readers by delivering powerful analysis and reporting.

Related Posts

Leave a Reply

You Missed

Malawi Awards Multimillion $ Passport Printing Contract To A Blacklisted Coy

Malawi Awards Multimillion $ Passport Printing Contract To A Blacklisted Coy

DPP’ Gangata Dates Dwangwa As He Takes Over MCP’ Bases

DPP’ Gangata Dates Dwangwa As He Takes Over MCP’ Bases

MEC Spends K23 Million Shipping Election Materials to Panama Amid Smartmatic Controversy

MEC Spends K23 Million Shipping Election Materials to Panama Amid Smartmatic Controversy

‘ IG ‘Ackis Muwanga Eliminates Opponents Ahead of Malawi Police Easter Promotions

‘ IG ‘Ackis Muwanga Eliminates Opponents Ahead of Malawi Police Easter Promotions