DK Pays MK 20 Million Nomination Fee For UTM Presidency

Times360Malawi

A Kabambe omwe apeleka cheke cha K20 million ati nthumwi zikawavotere chifukwa iwo all ndi ukadaulo oyendetsa chuma cha chipani komanso cha dziko.

A Kabambe omwe anali mkulu wa banki yaikulu ya dziko lino ati boma lomwe lilipo pakadali pano lalephera kuyendetsa chuma cha dziko.

“Panopa osauka akusaukirabe, anthu alibe chakudya. Mvulanso yayamba koma alibe feteleza. Omwe ali ndi galimoto ndiye akugona mma filling station nawo mavuto okhaokha. This government is clueless, it doesn’t know a anything and that’s why they say running government is not for babies,” atero a Kabambe.

A Kabambe, atinnso anthu mu chipani cha UTM abwere pamodzi ndikupanga kampeni yovuta kuti chaka cha mawa atenge boma.

“Amalawi ayesapo zipani zina, zalephera. Pano yesani UTM. Ine Dalitso Kabambe lero ndapeleka zikalata zosonyeza chidwi kupikisana, ndili ndi ukadaulo oyendetsa chuma cha dziko ndipo zinthu zambiri zomwe boma ili likupanga molakwikwa, mayankho ake ndili nawo,” atero a Kabambe.

Malawi Cables

Malawi Cables is a dedicated news platform providing timely and accurate coverage of events and stories from Malawi and beyond. The website aims to inform and engage readers by delivering powerful analysis and reporting.

Related Posts

Leave a Reply

You Missed

MCP Hires Hacker Jayson E. Street in Desperate Vote Rigging Scheme

MCP Hires Hacker Jayson E. Street in Desperate Vote Rigging Scheme

MCP Engages Senegalese Prof. Momar Dieng , Mpani In Election Rigging Scheme

MCP Engages Senegalese Prof. Momar Dieng , Mpani In Election Rigging Scheme

SLEEPY, PUPPET CHAKWERA BOWS TO SON’S PRESSURE, EYES MUMBA AS RUNNING MATE, 2030 SUCCESSOR

SLEEPY, PUPPET CHAKWERA BOWS TO SON’S PRESSURE, EYES MUMBA AS RUNNING MATE, 2030 SUCCESSOR

Usi Sparks Outrage at Mulli Funeral: Accused of Turning Burial into Political Stage

Usi Sparks Outrage at Mulli Funeral: Accused of Turning Burial into Political Stage