Chakwera’a Bloody Maize Donation Claims Life of Seven

A Polisi ya Ndirande mu mzinda wa Blantyre ati anthu okwana 7 ndi omwe amwalira pa ngozi imene yachitika mu msewu wa Magalasi chaku madzuloku.

Anthuwa amachokera ku bwalo la masewero la Kamuzu kumene adakalandira chimanga chimene bungwe la Dodma likupereka kwa anthu.

Malinga ndi wofalitsa nkhani pa polisi ya Ndirande a Maxwell Jailosi, galimotoyi idanyamula anthu okwana 37 ndipo mwa anthuwa awiri ndi amene avulala modetsa nkhawa pamene asanu awathandiza ndipo awatulutsa.

Galimoto ya mtundu wa lorry limene anthuwa adakwera, malinga ndi amene adaona izi zikuchitika a Isaac Chilenje, lidaonongeka mabuleki zimene zidachititsa kuti lithamange kwambiri lisadagwe.

Malawi Cables

Malawi Cables is a dedicated news platform providing timely and accurate coverage of events and stories from Malawi and beyond. The website aims to inform and engage readers by delivering powerful analysis and reporting.

Related Posts

Leave a Reply

You Missed

MCP Hires Hacker Jayson E. Street in Desperate Vote Rigging Scheme

MCP Hires Hacker Jayson E. Street in Desperate Vote Rigging Scheme

MCP Engages Senegalese Prof. Momar Dieng , Mpani In Election Rigging Scheme

MCP Engages Senegalese Prof. Momar Dieng , Mpani In Election Rigging Scheme

SLEEPY, PUPPET CHAKWERA BOWS TO SON’S PRESSURE, EYES MUMBA AS RUNNING MATE, 2030 SUCCESSOR

SLEEPY, PUPPET CHAKWERA BOWS TO SON’S PRESSURE, EYES MUMBA AS RUNNING MATE, 2030 SUCCESSOR

Usi Sparks Outrage at Mulli Funeral: Accused of Turning Burial into Political Stage

Usi Sparks Outrage at Mulli Funeral: Accused of Turning Burial into Political Stage